Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w06 3/15 tsamba 32
  • Dzasonkhaneni Nafe Lachitatu, pa April 12

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dzasonkhaneni Nafe Lachitatu, pa April 12
  • Nsanja ya Olonda—2006
Nsanja ya Olonda—2006
w06 3/15 tsamba 32

Dzasonkhaneni Nafe Lachitatu, pa April 12

Tsiku Lofunika Kulikumbukira

Usiku, patsiku lomwe anaphedwa, Yesu Kristu anakhazikitsa Chikumbutso cha imfa yake. Yesu anagwiritsira ntchito vinyo ndi mkate wopanda chotupitsa m’njira yophiphiritsira ndipo analamula kuti: “Chitani ichi chikumbukiro changa.”​—Luka 22:19.

Pomvera lamulo la Yesuli, Mboni za Yehova zikukuitanani kuti mukakhale nawo pa mwambo wa chaka n’chaka umenewu. Onani kuseri kwa kapepalaka kapena funsani Mboni za Yehova kwanuko kuti mudziwe malo, tsiku ndi nthawi ya msonkhanowu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena