Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w07 3/1 tsamba 32
  • Mwambo Wofunika Kukumbukira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mwambo Wofunika Kukumbukira
  • Nsanja ya Olonda—2007
Nsanja ya Olonda—2007
w07 3/1 tsamba 32

Mwambo Wofunika Kukumbukira

Lolemba, pa April 2

Pa Nisani 14, m’chaka cha 33 C.E., Yesu anagawira atumwi ake chikho cha vinyo ndi mtanda wa mkate wosafufumitsa. Atatero anawalangiza kuti: “Muzichita zimenezi pondikumbukira ine.”​—Luka 22:19.

Choncho, Mboni za Yehova padziko lonse zimasonkhana kamodzi pachaka kuti zikumbukire imfa ya Yesu. Amachita zimenezi potsatira malangizo amene Yesu anapereka tsiku limenelo. Chaka chino, tsiku la Nisani 14 lidzayamba Lolemba, pa April 2, dzuwa litalowa. Tikukuitanani kuti mudzakhale nafe pamsonkhanowu pokumbukira imfa ya Yesu. Tikukupemphani kuti mufunse nthawi ndi malo kwa Mboni za Yehova kwanuko.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena