Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w08 4/1 tsamba 32
  • Kodi Ndani Ali Woyenerera Kulamulira Anthu Onse?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Ndani Ali Woyenerera Kulamulira Anthu Onse?
  • Nsanja ya Olonda—2008
Nsanja ya Olonda—2008
w08 4/1 tsamba 32

Nkhani ya Onse Yapadera

Kodi Ndani Ali Woyenerera Kulamulira Anthu Onse?

Kodi ndi wolamulira uti amene angachite izi:

• kuthetsa mavuto azachuma, njala ndiponso kupangitsa kuti anthu onse akhale ndi nyumba zabwino?

• kuthetsa masoka achilengedwe, kuti anthu asamavutike ndi matsunami, mphepo za mkuntho kapena zivomezi?

• kuthetsa matenda onse ngakhalenso kuchititsa anthu okalamba kukhalanso anyamata?

• kuthetsa nkhondo zonse kuti anthu onse azikhala mwabata ndi mtendere?

• kubwezeretsa chilengedwe chonse kuti chikhalenso mmene chinalili poyamba ndi kusintha dziko lonse kukhala paradaiso?

Pali Wolamulira mmodzi yekha amene angachite zimenezi. Kodi iye ndani? Funso limeneli lidzayankhidwa m’nkhani ya onse yapadera ya mutu wakuti: “Kodi Ndani Ali Woyenerera Kulamulira Anthu Onse?” Nkhani imeneyi idzakambidwa padziko lonse m’mayiko oposa 230. M’madera ambiri nkhaniyi idzakambidwa pa Nyumba ya Ufumu ya Mboni za Yehova, Lamlungu, April 6, 2008. Mboni za kwanuko n’zokonzeka ndipo zidzasangalala kukuuzani nthawi ndi malo kumene nkhaniyi idzakambidwire. Tikukuitanani ndi mtima wonse kuti mudzapezekepo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena