Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w10 8/1 tsamba 32
  • Tsamba 32

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tsamba 32
  • Nsanja ya Olonda—2010
Nsanja ya Olonda—2010
w10 8/1 tsamba 32

Tsamba 32

Kodi dziko lapansili lidzawonongedwa? ONANI TSAMBA 5.

Malinga ndi zimene Babulo limanena, kodi Mulungu adzathetsa chiyani? ONANI MASAMBA 5-6.

Mukakhumudwa ndi zimene mkazi kapena mwamuna wanu wachita, kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuti mumulankhule mwaulemu? ONANI TSAMBA 12.

Kodi Yesu ananena kuti n’chiyani chingapangitse munthu kukhala wosangalala? ONANI TSAMBA 16.

Kodi n’kutheka kuti ntchito ya Yesu monga mmisiri wa matabwa inakhudza bwanji zimene ankaphunzitsa? ONANI MASAMBA 25-26.

[Mawu a Chithunzi patsamba 32]

U.S. National Archives photo

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena