Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w11 2/1 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2011
Nsanja ya Olonda—2011
w11 2/1 tsamba 1-2

Zamkatimu

February 1, 2011

Kodi Mungatani Kuti Banja Lanu Likhale Lolimba?

NKHANI ZOYAMBIRIRA

3 N’chifukwa Chiyani Mabanja Ambiri Akutha?

4 Malangizo Othandiza pa Zimene Amuna Komanso Akazi Ambiri Amadandaula

• “Ine ndi mwamuna (kapena mkazi) wanga sitikuchitiranso zinthu limodzi ndipo sitikukondana ngati kale”

• “Palibenso phindu lililonse limene ndikupeza m’banja”

• “Mwamuna (kapena mkazi) wanga sachita zimene amayenera kuchita”

• “Mkazi wanga samandimvera”

• “Mwamuna wanga sachita zinthu ngati mwamuna”

• “Zimene mwamuna (kapena mkazi) wanga amachita zimandikwiyitsa ndipo zanditopetsa”

NKHANI ZA NTHAWI ZONSE

10 Baibulo Limasintha Anthu

14 Yandikirani Mulungu​—“Inu Mulungu Wanga, Mundikumbukire pa Zabwino Zimene Ndinachita”

15 Kodi Mukudziwa?

16 Phunzirani Zimene Mawu a Mulungu Amanena​—Kodi Mulungu Ndani?

18 Chinsinsi cha Banja Losangalala​—Muziphunzitsa Ana Anu Makhalidwe Abwino

25 Phunzitsani Ana Anu​—Ankakondedwa ndi Mulungu Komanso Anzake

27 Zimene Owerenga Amafunsa

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI:

21 Kodi Mukukonzekera Tsiku Lofunika Kwambiri Chaka Chino?

28 “Lero Ndi Tsiku Limene Mwakhala Mukuliyembekezera”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena