Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w16 June tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
w16 June tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Yehova “Amakuderani Nkhawa”

MLUNGU WA AUGUST 1-7, 2016

6 Tiziyamikira Kuti Yehova Amatiumba

MLUNGU WA AUGUST 8-14, 2016

11 Kodi Mumalola Kuti Yehova Azikuumbani?

Munthu akamaumba chinthu, amakhala nacho pafupi kwambiri. M’nkhani ziwirizi, tiona mmene Yehova amatiumbira komanso zimene tingachite kuti tikhale ngati dongo labwino.

16 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

MLUNGU WA AUGUST 15-21, 2016

18 “Yehova Mulungu Wathu Ndi Yehova Mmodzi”

Kodi mawu oti Yehova Mulungu wathu ndi “Yehova mmodzi” amatanthauza chiyani? Nanga zimenezi zimakhudza bwanji ubwenzi wathu ndi iye komanso ndi Akhristu anzathu? Popeza m’dzikoli muli anthu amitundu komanso zikhalidwe zosiyanasiyana, tiyenera kumvetsa bwino zimene Yehova amafuna kuti tizichita n’cholinga choti akhale “Mulungu wathu.”

MLUNGU WA AUGUST 22-28, 2016

23 Tisasiye Kutumikira Mulungu Chifukwa cha Zochita za Ena

Tonsefe nthawi zina timakhumudwitsa anzathu. Kodi ndi zitsanzo za m’Baibulo ziti zomwe zingatithandize kudziwa zoyenera kuchita ena akalankhula kapena kuchita zinthu zotikhumudwitsa?

28 Khalidwe la Mtengo Wapatali Kuposa Dayamondi

32 Kodi Mukukumbukira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena