Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 July tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 July tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Anadzipereka Ndi Mtima Wonse—Ku Turkey

MLUNGU WA AUGUST 28, 2017—SEPTEMBER 3, 2017

7 Muzifunafuna Chuma Chenicheni

Nkhaniyi ikufotokoza mmene tingagwiritsire ntchito chuma chathu kuti ‘tipeze mabwenzi’ kumwamba. (Luka 16:9) Ikufotokozanso zimene zingatithandize kuti tisakhale akapolo a ndalama komanso kuti tizitumikira Yehova mwakhama.

MLUNGU WA SEPTEMBER 4-10, 2017

12 “Lirani ndi Anthu Amene Akulira”

Kodi n’chiyani chingathandize anthu amene aferedwa? Yehova amalimbikitsa anthu oterewa pogwiritsa ntchito Yesu Khristu, Malemba komanso mpingo wachikhristu. Nkhaniyi ikufotokoza zimene zingalimbikitse munthu amene waferedwa komanso mmene anthu ena angamuthandizire.

MLUNGU WA SEPTEMBER 11-17, 2017

17 N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kutamanda Yehova?

Salimo 147 limalimbikitsa anthu a Mulungu mobwerezabwereza kuti azitamanda Yehova. Kodi n’chifukwa chiyani munthu amene analemba salimoli ankafuna kuti Mulungu azitamandidwa? Nkhaniyi iyankha funsoli komanso ifotokoza chifukwa chake ifenso tiyenera kukhala ofunitsitsa kutamanda Mulungu.

MLUNGU WA SEPTEMBER 18-24, 2017

22 ‘Mulungu Akwaniritse Zofuna Zanu’

Abale ndi alongo ambiri akuchita utumiki wa nthawi zonse ali achinyamata. Kodi inunso muli ndi cholinga chimenechi? Munkhaniyi muli malangizo abwino ochokera m’Malemba omwe angakuthandizeni kudzakhala ndi tsogolo labwino.

27 Tetezani Maganizo Anu

31 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena