Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w17 August tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
w17 August tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA SEPTEMBER 25, 2017–OCTOBER 1, 2017

3 Kodi Mukhoza Kuyembekezera Moleza Mtima?

MLUNGU WA OCTOBER 2-8, 2017

8 ‘Mtendere wa Mulungu Umaposa Kuganiza Mozama Kulikonse’

Nkhani yoyamba ikufotokoza chifukwa chake tiyenera kuyembekezera Yehova. Tionanso kuti zitsanzo za amuna ndi akazi okhulupirika akale zingatithandize kuti tizidikira moleza mtima. Nkhani yachiwiri ikusonyeza kuti Yehova akhoza kuchita zinthu zimene sitikuyembekezera. Nkhaniyi ingatithandize kumukhulupirira n’kumadikira moleza mtima kuti atithandize.

13 Mbiri ya Moyo Wanga​—Tikapirira Mavuto Tidzadalitsidwa

MLUNGU WA OCTOBER 9-15, 2017

17 Vulani Umunthu Wakale Ndipo Musauvalenso

MLUNGU WA OCTOBER 16-22, 2017

22 Valani Umunthu Watsopano Ndipo Musauvulenso

Nkhani yoyamba ikufotokoza tanthauzo la kuvula umunthu wakale komanso chifukwa chake tiyenera kuchita zimenezi mwamsanga. Ikufotokozanso zimene tingachite kuti tisauvalenso. Nkhani yachiwiri ikufotokoza makhalidwe angapo omwe amapanga umunthu watsopano. Ikufotokozanso mmene tingasonyezere makhalidwewa pa moyo wathu komanso mu utumiki.

27 Chikondi Ndi Khalidwe Lamtengo Wapatali Kwambiri

30 Kale Lathu

32 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena