Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 June tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 June tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’Magaziniyi

MLUNGU WA AUGUST 6-12, 2018

3 “Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino”

MLUNGU WA AUGUST 13-19, 2018

8 Tonsefe Tikhale Ogwirizana Ngati Yehova ndi Yesu

Anthu m’nthawi ya Yesu anali ogawikana chifukwa chosiyana pa nkhani ya ndale, maudindo komanso mitundu. Nkhani ziwirizi zikusonyeza zimene Yesu anaphunzitsa ophunzira ake kuti akhale ogwirizana ndiponso azipewa tsankho limene limagawanitsa anthu. Popeza anthu ambiri m’dzikoli sagwirizana, tionanso mmene chitsanzo cha ophunzirawo chingatithandizire.

13 Akanatha Kusangalatsa Mulungu

MLUNGU WA AUGUST 20-26, 2018

16 Muziphunzitsa Chikumbumtima Chanu ndi Malamulo Komanso Mfundo za Mulungu

Kuti chikumbumtima chathu chizititsogolera bwino tiyenera kuchiphunzitsa. Yehova watipatsa malamulo komanso mfundo zimene zingatithandize kuphunzitsa chikumbumtima chathu komanso kuona zinthu mmene iye amazionera. Nkhaniyi ikufotokoza mmene tingagwiritsire ntchito bwino mfundo za m’Baibulo.

MLUNGU WA AUGUST 27, 2018–SEPTEMBER 2, 2018

21 “Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke

Yesu anauza ophunzira ake kuti azionetsa kuwala kwawo kuti Mulungu alemekezeke. Nkhaniyi ikufotokoza zinthu zimene zingatithandize kuti tizionetsa kwambiri kuwala kwathu.

26 Mbiri ya Moyo Wanga​—Ndakhala Ndikulimbikitsidwa pa Mavuto Anga Onse

30 Kupatsana Moni N’kothandiza Kwambiri

32 Kodi Mukukumbukira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena