Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 July tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 July tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Anadzipereka ndi Mtima Wonse—Ku Myanmar

MLUNGU WA SEPTEMBER 3-9, 2018

7 Kodi Mumafuna Kukhala Wodziwika kwa Ndani?

Anthu ambiri amafuna kukhala odziwika m’dziko loipali. Munkhaniyi tikambirana zimene tingachite kuti tikhale odziwika kwa Yehova n’kumapeza madalitso amene iye amapereka kwa atumiki ake okhulupirika. Tionanso kuti nthawi zina anthu odziwika kwa Yehova amadalitsidwa m’njira imene sankayembekezera.

MLUNGU WA SEPTEMBER 10-16, 2018

12 Kodi Maso Anu Amayang’ana kwa Ndani?

Munkhaniyi tiona chifukwa chimene chinachititsa kuti Mose, yemwe anali wokhulupirika, alephere kulowa m’Dziko Lolonjezedwa. Tionanso mmene tingapewere zimene zinachitikira Mose.

MLUNGU WA SEPTEMBER 17-23, 2018

17 “Ndani Ali Kumbali ya Yehova?”

MLUNGU WA SEPTEMBER 24-30, 2018

22 Ndife Anthu a Yehova

Anthu onse padzikoli analengedwa ndi Yehova. Choncho tiyenera kukhala odzipereka kwa iye yekha. Anthu ena amanena kuti ndi okhulupirika kwa Mulungu koma kwinaku akuchita zinthu zosamumvera. Munkhani yoyamba tikambirana zimene tikuphunzira kwa Kaini, Solomo, Mose ndi Aroni. Munkhani yachiwiri tikambirana zimene tingachite posonyeza kuti timayamikira mwayi wokhala anthu a Yehova.

27 Muzichitira Chifundo Anthu “Kaya Akhale a Mtundu Wotani”

30 Kodi Mungatani Kuti Kuphunzira Baibulo Kuzikusangalatsani Komanso Kuzikuthandizani?

32 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena