Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 October tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 October tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

3 Zimene Zinachitika Zaka 100 Zapitazo mu 1918

MLUNGU WA DECEMBER 3-9, 2018

6 Tizilankhula Zoona Zokhazokha

MLUNGU WA DECEMBER 10-16, 2018

11 Tiziphunzitsa Mfundo za Choonadi

Masiku ano anthu ambiri amakonda kunama. Koma kodi kunama kunayamba bwanji? Nanga bodza loipa kwambiri limene linanenedwapo ndi liti? Kodi tingapewe bwanji kupusitsidwa ndi anthu ena, nanga tingasonyeze bwanji kuti timalankhula zoona zokhazokha? Kodi Zinthu Zomwe Timagwiritsa Ntchito Pophunzitsa zingatithandize bwanji mu utumiki? Nkhanizi ziyankha mafunso onsewa.

17 Mbiri ya Moyo Wanga​—Yehova Wandidalitsa Kwambiri Chifukwa cha Zimene Ndinasankha

MLUNGU WA DECEMBER 17-23, 2018

22 Tizikhulupirira Khristu Yemwe Ndi Mtsogoleri Wathu

MLUNGU WA DECEMBER 24-30, 2018

27 Tizikhalabe ndi Mtendere Wamumtima Zinthu Zikasintha

Popeza si ife angwiro, timavutika kuvomereza zinthu zikasintha pa moyo wathu kapena m’gulu la Yehova. Nkhani ziwirizi zitithandiza kuti tizikhala ndi mtendere wamumtima komanso tizidalira Mtsogoleri wathu Yesu Khristu ngakhale pamene zinthu pa moyo wathu zasintha mosayembekezereka.

32 Kodi Mukudziwa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena