Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w18 November tsamba 2
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
w18 November tsamba 2

Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi

MLUNGU WA DECEMBER 31, 2018–JANUARY 6, 2019

3 “Gula Choonadi Ndipo Usachigulitse”

MLUNGU WA JANUARY 7-13, 2019

8 “Ndidzayenda M’choonadi Chanu”

Nkhani ziwirizi zitithandiza kuona kuti choonadi ndi mphatso yamtengo wapatali imene Yehova watipatsa. Choonadi ndi chamtengo wapatali kwambiri kuposa chinthu chilichonse chimene timalolera kusiya kuti tipeze choonadicho. Nkhanizi zitithandizanso kuti tisasiye kuona kuti choonadi ndi chamtengo wapatali komanso kuti tisayerekeze n’komwe kugulitsa mfundo ya choonadi iliyonse imene Yehova watiphunzitsa.

MLUNGU WA JANUARY 14-20, 2019

13 Muzikhulupirira Yehova Kuti Mukhale ndi Moyo

Buku la Habakuku lili ndi mfundo zotithandiza kuti tizikhulupirira Yehova pa nthawi imene tikukumana ndi mavuto. Nkhaniyi itithandiza kudziwa kuti tikamakhulupirira Yehova pa nthawi imene tikukumana ndi mavuto osiyanasiyana iye adzatipulumutsa.

MLUNGU WA JANUARY 21-27, 2019

18 Kodi Mumayendera Maganizo a Ndani?

MLUNGU WA JANUARY 28, 2019–FEBRUARY 3, 2019

23 Tiziyendera Maganizo a Yehova

Munthu akamakula mwauzimu amazindikira kuti maganizo a Yehova ndi apamwamba kwambiri. Nkhani ziwirizi zitithandiza kuti tisamayendere maganizo a anthu a m’dzikoli koma tiziyendera maganizo a Yehova.

28 Kukoma Mtima Ndi Khalidwe Limene Limasonyezedwa M’mawu ndi Zochita

31 Mafunso Ochokera kwa Owerenga

32 Kodi Ndingapereke Chiyani kwa Yehova?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena