Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w19 December tsamba 32
  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw Library Komanso Jw.Org

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw Library Komanso Jw.Org
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
w19 December tsamba 32

Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw Library Komanso Jw.Org

ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA

Ndingatani Kuti Ndizigawa Bwino Nthawi Yanga?

Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzigwiritsa ntchito bwino nthawi yanu.

Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > YOUNG PEOPLE ASK.

Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.

KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

Guluu wa Kanyama Kotchedwa Barnacle

Guluu wa kanyamaka amamata mwamphamvu kwambiri kuposa guluu aliyense wopangidwa ndi anthu. Posachedwapa, asayansi atulukira zimene zimathandiza kuti azimata kwambiri pamalo pamene pali madzi.

Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > WAS IT DESIGNED?

Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > BAIBULO KOMANSO SAYANSI > KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena