Nkhani Zimene Zatuluka Pa Jw Library Komanso Jw.Org
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Ndingatani Kuti Ndizigawa Bwino Nthawi Yanga?
Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzigwiritsa ntchito bwino nthawi yanu.
Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > YOUNG PEOPLE ASK.
Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > ACHINYAMATA > ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA.
KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?
Guluu wa Kanyama Kotchedwa Barnacle
Guluu wa kanyamaka amamata mwamphamvu kwambiri kuposa guluu aliyense wopangidwa ndi anthu. Posachedwapa, asayansi atulukira zimene zimathandiza kuti azimata kwambiri pamalo pamene pali madzi.
Pa JW Library, pitani pamene alemba kuti PUBLICATIONS > ARTICLE SERIES > WAS IT DESIGNED?
Pa jw.org, pitani pamene alemba kuti ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA > BAIBULO KOMANSO SAYANSI > KODI ZINANGOCHITIKA ZOKHA?