Zilengezo
◼ Mabuku ogaŵira mu May: Makope a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! June: Lililonse la mabuku otsatirawa a masamba 192 limene mpingo ungakhale nalo m’sitoko: Chisungiko cha Padziko Lonse mu Ulamuliro wa “Kalonga wa Mtendere,” Happiness—How to Find It, Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo, Kupulumuka Kuloŵa m’Dziko Latsopano, “Let Your Kingdom Come,” Mtendere Weniweni ndi Chisungiko—Kodi Mungazipeze Motani?, Ogwirizana m’Kulambiridwa kwa Mulungu Yekha Wowona, ndi Your Youth—Getting the Best Out Of It. July ndi August: Mungagwiritsire ntchito lililonse la mabrosha otsatirawa a masamba 32: Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso, Kodi Chifuno cha Moyo Nchiyani—Kodi Mungachipeze Motani?, Kodi Mulungu Amatisamaliradi?, Kodi Muyenera Kukhulupirira Utatu?, Pamene Munthu Amene Mumakonda Amwalira, ndi Sangalalani ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha! Mabrosha akuti Buku la Anthu Onse, Mizimu ya Akufa—Kodi Ingakuthandizeni Kapena Kukuvulazani? Kodi Iyo Ilikodi?, Our Prolems—Who Will Help Us Solve Them?, ndi Will There Ever Be a World Without War? mungawagaŵire pamene kuli koyenera.
◼ Zofalitsa Zomwe Zilipo:
Chidziŵitso Chotsogolera ku Moyo Wosatha—Chitumbuka
Kesi Yosungiramo Magazini
Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife?—Chingelezi
New World Translation of the Holy Scriptures (Saizi yapakati; DLbi12) lakuda—Chingelezi
Olinganizidwa Kutsiriza Uminisitala Wathu—Chingelezi
Bukhu Lolangiza la Sukulu Yateokratiki—Cingelezi
◼ Makompakiti Disiki Atsopano Omwe Alipo:
Kingdom Melodies, Voliyumu 6