Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/11 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 6/11 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

N’zosangalatsa kwambiri kuona kuti Yehova akutidalitsa chifukwa cha khama limene tikuchita posonkhanitsa anthu okhala ngati nkhosa m’gawo lathu. Kwa nthawi yoyamba, m’mwezi wa December 2010, ofalitsa onse tinakwana 79,157. Tiyeni tipitirize kulalikira mwakhama kuti tipeze anthu ambiri amene akufunafuna choonadi ndiponso kuti tiwathandiza mapeto a nthawi ino asanafike.—Mat. 28:19, 20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena