Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 7/11 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 7/11 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

M’mwezi wa February chaka chino, tinachititsa maphunziro a Baibulo okwana 86,680. Umenewu ndi umboni wakuti pali anthu ambiri amene akuusa moyo ndi kubuula chifukwa cha zonyansa zonse zimene zikuchitika m’dzikoli masiku ano. (Ezek. 9:4) Tikufunanso kuthokoza aliyense chifukwa takhala tikulandira malipoti pa nthawi yake kwa miyezi itatu yapitayi. Tipezerepo mwayi wodziwitsa akulu kuti muziyesetsa kutumiza malipoti ku ofesi ya nthambi pa galimoto ya Sosaite m’malo motumiza papositi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena