Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/11 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
km 9/11 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Mwezi wa April, womwe tinachitanso Chikumbutso, tinagawira mabuku ndi timabuku 188,129. Tinagawiranso magazini okwana 492,454. Kuwonjezera pamenepa, tinachititsa maphunziro a Baibulo okwana 99,640 ndipo tinathera maola 1,384,091 mu utumiki wakumunda. M’mwezi umenewunso abale ndi alongo 8,033 anadzipereka kuchita upainiya wothandiza. Tikukuthokozani kwambiri abale chifukwa cha khama lanu pa nyengo ya Chikumbutso. Sitikukayikira kuti Yehova apitiriza kudalitsa khama lathu pamene tikumvera lamulo la Yesu loti tizilalikira ndi kuthandiza anthu kuti akhale ophunzira ake.—Mat. 28:19-20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena