Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 4/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Posachedwapa, m’bale wina anayamikira kwambiri ntchito yophunzitsa anthu Baibulo. Iye anati: “Ndakhala ndikugwira ntchito kwa zaka 26 ngati wapolisi. Ndinaphunzira zambiri zokhudza chitetezo koma tsopano ndikuona kuti ndinaphunzira zinthu zochepa kwambiri ndikayerekezera ndi zimene ndaphunzitsidwa ndi gulu la Yehova za chitetezo chenicheni.” Panopo munthu ameneyu anasiya ntchito ya polisi. Iye ndi m’bale wobatizidwa ndipo akugwira nawo ntchito yophunzitsa anthu Baibulo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena