Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/12 tsamba 4
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 8/12 tsamba 4

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira mu August: Ofalitsa angagawire timabuku totsatirati: Kodi Baibulo Lili Ndi Uthenga Wotani?, kapena kakuti, Moyo Wokhutiritsa—Mmene Mungaupezere. Popanga maulendo obwereza, sonyezani mwininyumba buku lakuti, Baibulo Limaphunzitsa Chiyani ndipo muyesetse kuyambitsa phunziro la Baibulo. September ndi October: Gawirani magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! Pochita maulendo obwereza, mungayambitse phunziro la Baibulo pogwiritsira ntchito buku lakuti, Baibulo Limaphunzitsa Chiyani. November: Ofalitsa angagawire timapepala totsatirati: Mavuto Onse a Anthu Adzatha Posachedwapa, Yehova—Kodi Iye Ndani?, Yesu Khristu—Kodi Iye Ndani?, kapena Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi? Ngati mwapeza anthu achidwi, asonyezeni mmene timaphunzirira Baibulo pogwiritsa ntchito buku lakuti, Baibulo Limaphunzitsa Chiyani kapena timabuku takuti Mverani Mulungu ndiponso Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena