Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/12 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 11/12 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Mwezi wa June chaka chino, tinathera maola 1,268,035 pa ntchito yophunzitsa anthu zokhudza Ufumu wa Mulungu. Zimenezi zikusonyeza kuti wofalitsa aliyense anathera maola pafupifupi 16 ali mu utumiki wakumunda. Tikukuyamikirani kwambiri abale ndi alongo chifukwa chogwira ntchito yolalikira ‘uthenga wabwino wa ufumu’ mwakhama ngakhale kuti mukukumana ndi mavuto osiyanasiyana.—Mat. 24:14; 28:19, 20.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena