Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/12 tsamba 8
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
km 12/12 tsamba 8

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Nyumba ya Ufumu ya mpingo wa Milombwa m’dera la C-04 inamalizidwa kumangidwa pa February 16, 2012. Malipoti akusonyeza kuti pamene abale ndi alongo ankamanga Nyumba ya Ufumuyi, tsiku lililonse anthu pafupifupi 42, omwe si Mboni, ankabwera kudzaona mmene ntchitoyi inkayendera. Anthu ambiri anachita chidwi chifukwa cha kugwirizana ndiponso kugwira ntchito kwathu mwakhama. Pakali pano m’Malawi muno muli Nyumba za Ufumu zoposa 1,060. Zimenezi zikusonyeza kuti Mulungu wathu Yehova ndi wowolowa manja ndipo tikumuthokoza chifukwa chopereka malo abwino olambirira amenewa kwa anthu ake mopanda tsankho.—Mac. 10:34, 35.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena