Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 3/14 tsamba 4
  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zochitika mu Utumiki Wakumunda
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 3/14 tsamba 4

Zochitika mu Utumiki Wakumunda

Kwa nthawi yoyamba m’Malawi, mabanja 10 ochokera m’dziko lathu lino komanso mabanja awiri ochokera ku Mozambique anachita mwambo womaliza maphunziro awo. Anachita mwambowu ataphunzira kwa miyezi iwiri m’kalasi yoyamba ya Sukulu Yophunzitsa Baibulo ya Akhristu Apabanja imene inachitika m’Chichewa. Mwambowu unachitika Lamlungu pa October 27, 2013. N’zosakayikitsa kuti mabanja amenewa akathandiza mipingo imene atumizidwako. Tikukhulupiriranso kuti mabanja ambiri akonza zoti adzalowe sukuluyi m’tsogolomu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena