Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 9/14 tsamba 4
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 9/14 tsamba 4

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira mu September ndi October: Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! November ndi December: Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? kapena kapepala kakuti, Kodi Mukufuna Kudziwa Choonadi?

◼ Nkhani yapadera ya panyengo ya Chikumbutso cha 2015 idzakambidwa pa mlungu woyambira April 6. Mutu wa nkhaniyi tidzakudziwitsanibe. Mipingo imene idzakhale ndi mlungu wapadera kapena msonkhano pa mlungu umenewu, idzakambe nkhaniyi mlungu wotsatira. Dziwani kuti nkhaniyi siyenera kukambidwa mlungu wa April 6 usanafike.

◼ Kuyambira mwezi wa September, oyang’anira dera azidzakamba nkhani ya mutu wakuti, “Kodi Nzeru Yochokera kwa Mulungu Ingatithandize Bwanji?”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena