Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsamba 4
  • Zilengezo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zilengezo
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsamba 4

Zilengezo

◼ Mabuku ogawira mu August: Timabuku takuti, Mverani Mulungu, Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha ndi Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu. September ndi October: Magazini a Nsanja ya Olonda ndi Galamukani! November: Buku lakuti, Kodi Baibulo Limaphunzitsa Chiyani Kwenikweni? kapena timapepala tatsopano totsatirati: Kodi Baibulo Mumalikhulupirira?, Kodi Dziko Lapansili Lili M’manja mwa Ndani?, Kodi Mavuto Amene Tikukumana Nawowa Adzathadi?, Kodi Mukuganiza Kuti Zinthu Zidzakhala Bwanji M’tsogolo?, Kodi N’chiyani Chingathandize Kuti Banja Likhale Losangalala?, Kodi N’zoonadi Kuti Akufa Adzauka? ndi kakuti, Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?

◼ Kuyambira mu September, woyang’anira dera azidzakamba nkhani ya onse ya mutu wakuti, “Kodi Malangizo a Mulungu Ndi Othandizadi?”

◼ Makalasi Ophunzitsa Kuwerenga ndi Kulemba: Ngati sukuluyi sikuchitika mumpingo mwanu, konzani zoti iyambe n’cholinga choti muthandize abale ndi alongo omwe sadziwa kulemba ndi kuwerenga. Izi zingawathandize kuti azitha kuwerenga okha Baibulo komanso mabuku athu. Zingawathandizenso kuti aziphunzitsa ana awo mogwira mtima.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena