Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 February tsamba 6
  • Zimene Tikuphunzira kwa Nehemiya

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tikuphunzira kwa Nehemiya
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Mwapatulidwa
    Nsanja ya Olonda—2013
  • “Pitirizani Kugonjetsa Choipa mwa Kuchita Chabwino”
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Mfundo Zazikulu za M’buku la Nehemiya
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Inu Mulungu Wanga, Mundikumbukire pa Zabwino Zimene Ndinachita”
    Nsanja ya Olonda—2011
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 February tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | NEHEMIYA 12-13

Zimene Tikuphunzira kwa Nehemiya

Nehemiya anali wakhama poteteza kulambira koona

13:4-9, 15-21, 23-27

Nehemiya akutaya katundu wa Tobiya panja pa kachisi
  • Mkulu wa ansembe dzina lake Eliyasibu analola kuyendera maganizo a Tobiya, yemwe sankalambira Yehova

  • Eliyasibu anakonzera Tobiya chipinda m’bwalo la nyumba ya Mulungu

  • Nehemiya anataya kunja katundu wa Tobiya n’kuyeretsa chipindacho kuti chizigwira ntchito yake yoyenera

  • Nehemiya anapitiriza kuyeretsa Yerusalemu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena