Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 4
  • August 8-14

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 8-14
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 4

August 8-14

MASALIMO 92-101

  • Nyimbo Na. 28 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mukhoza Kumachitabe Zambiri Ngakhale Muli Okalamba”: (10 min.)

    • Sal. 92:12—Olungama amabereka zipatso (w07 9/15 32; w06 7/15 13 ndime 2)

    • Sal. 92:13, 14—Okalamba akhoza kumachitabe zambiri ngakhale mphamvu zawo zili zochepa (w14 1/15 26 ndime 17; w04 5/15 12 ndime 9-10)

    • Sal. 92:15—Okalamba akhoza kulimbikitsa ena powafotokozera zomwe akumana nazo pa moyo wawo (w04 5/15 12-14 ndime 13-18)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Sal. 99:6, 7—N’chifukwa chiyani tinganene kuti Mose, Aroni komanso Samueli ndi zitsanzo zabwino? (w15 7/15 8 ndime 5)

    • Sal. 101:2—Kodi mawu akuti, “Ndidzayendayenda m’nyumba yanga ndi mtima wanga wosagawanika” akutanthauza chiyani? (w05 11/1 24 ndime 14)

    • Kodi ndaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo ziti zimene ndaphunzira pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno zimene ndingazigwiritse ntchito mu utumiki?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Sal. 95:1–96:13

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Tsamba loyamba la g16.4—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Tsamba loyamba la g16.4—Siyani funso loti mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bh 161-162 ndime 18-19—Thandizani wophunzirayo kuti aone mmene angagwiritsire ntchito mfundo za m’ndimezi.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 90

  • Achikulire—Ndinu Ofunika Kwambiri (Sal. 92:12-15): (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yamutu wakuti, Achikulire—Ndinu Ofunika Kwambiri. (Pitani pamene alemba kuti MAVIDIYO ENA > BAIBULO.) Kenako funsani abale ndi alongo kuti afotokoze zomwe tikuphunzirapo. Pemphani abale ndi alongo achikulire kuti azithandiza achinyamata kusankha zinthu mwanzeru komanso aziwafotokozera zomwe anakumana nazo pa moyo wawo. Limbikitsani achinyamata kuti azipempha achikulire kuti aziwathandiza maganizo akamasankha zinthu zofunika kwambiri.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) ia mutu 4 ndime 1-15, komanso bokosi patsamba 39.

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 29 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena