Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsamba 4
  • Anthu Akamatsogoleredwa ndi Yehova Zinthu Zimawayendera Bwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu Akamatsogoleredwa ndi Yehova Zinthu Zimawayendera Bwino
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2022
  • “Abusa Amene Mtima Wanga Wakonda”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Abusa Omwe Ndi ‘Zitsanzo kwa Gulu’ la Nkhosa
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Ine Ndili ndi Iwe Kuti Ndikulanditse”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 March tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 8-11

Anthu Akamatsogoleredwa ndi Yehova Zinthu Zimawayendera Bwino

Anthu alibe luso komanso ufulu woti azidzilamulira okha

10:21-23

  • Aisiraeli anabalalika chifukwa choti abusa awo sankafunafuna Yehova

    Abusa a Aisiraeli akupemphera kwa milungu yonyenga; Yerusalemu akuwonongedwa
  • Anthu amene ankatsatira malangizo a Yehova anali pa mtendere, ankakhala mosangalala komanso zinthu zinkawayendera bwino

    Mwamuna wachiisiraeli akuwerenga malamulo a Mulungu ndipo iye limodzi ndi banja lake ali pamtendere, ndi osangalala komanso zinthu zikuwayendera bwino
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena