Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 7
  • Yehova Amadalitsa Anthu Odzichepetsa Ndipo Amalanga Odzikuza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amadalitsa Anthu Odzichepetsa Ndipo Amalanga Odzikuza
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Babulo Wamphamvu—Mphamvu Yaikulu ya Dziko Yachitatu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Yehova Adzaweruza Aliyense Malinga ndi Ntchito Zake
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Mzinda Waukulu Udzawonongedwa
    Mapeto Osangalatsa a Masomphenya a M’buku la Chivumbulutso
  • Kodi Nkhanza Zidzathadi?
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 49-50

Yehova Amadalitsa Anthu Odzichepetsa Ndipo Amalanga Odzikuza

50:4-7

  • Aisiraeli omwe analapa anasangalala Yehova atawamasula ku ukapolo

  • Iwo anabwerezanso pangano lawo lomwe anachita ndi Yehova ndipo anabwerera ku Yerusalemu n’kukayambiranso kulambira Mulungu

    Aisiraeli akuchoka ku Babulo

50:29, 39

  • Ababulo omwe anali odzikuza, analangidwa chifukwa ankachitira nkhanza anthu a Yehova

  • Monga mmene ulosi unanenera, Babulo anakhala bwinja

    Munthu wodzikuza wa ku Babulo ndi mabwinja a Babulo momwe muli nyama za kutchire zokhazokha
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena