Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 July tsamba 4
  • July 17-23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 17-23
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 July tsamba 4

July 17-23

EZEKIELI 18-20

  • Nyimbo Na. 21 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Yehova Akatikhululukira Machimo, Amawakumbukirabe?”: (10 min.)

    • Ezek. 18:19, 20​—Yehova amaimba mlandu munthu aliyense malinga ndi zochita zake (w12 7/1 18 ¶2)

    • Ezek. 18:21, 22​—Yehova ndi wokonzeka kukhululukira anthu amene alapa ndipo akatero samawaimbanso mlandu (w12 7/1 18 ¶3-7)

    • Ezek. 18:23, 32​—Yehova amawononga oipa pokhapokha ngati wawachenjeza koma sakufuna kusintha (w08 4/1 8 ¶4; w06 12/1 27 ¶11)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 18:29​—N’chifukwa chiyani Aisiraeli anayamba kuganiza kuti Yehova akulakwitsa zinthu, nanga kodi ifeyo tingapewe bwanji mtima umenewu? (w13 8/15 11 ¶9)

    • Ezek. 20:49​—Kodi n’chifukwa chiyani anthu ankaganiza kuti Ezekieli ‘akunena miyambi,’ nanga ifeyo tikupezapo chenjezo lotani? (w07 7/1 14 ¶3)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 20:1-12

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) 1 Yoh. 5:19​—Kuphunzitsa Choonadi. Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Gen. 3:2-5​—Kuphunzitsa Choonadi. Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira. (Onani mwb16.08 8 ¶2.)

  • Nkhani: (Osapitirira 6 min.) w16.05 32​—Mutu: Kodi Tingasonyeze Bwanji Kusangalala Tikamva Chilengezo Choti Munthu Wina Wabwezeretsedwa?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 77

  • “Kodi Mumadziimbabe Mlandu Yehova Akakukhululukirani?”: (10 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonetsa vidiyo yakuti Muzitsatira Mokhulupirika Mfundo za Yehova​—Muzikhululuka.

  • Zimene Achinyamata Amadzifunsa​—Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake?: (5 min.) Kambiranani nkhani yakuti “Zimene Achinyamata Amadzifunsa​—Kodi Ndizitani Ndikalakwitsa Zinazake?” Yambani ndi kumvetsera nkhaniyi pa gawo lakuti “Kodi Inuyo Mungatani?”

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 4 ¶1-6, komanso tsamba 43

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena