Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 October tsamba 8
  • October 30–November 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 30–November 5
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 October tsamba 8

October 30–November 5

YOWELI 1-3

  • Nyimbo Na. 143 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Ana Anu Aamuna ndi Ana Anu Aakazi Adzanenera”: (10 min.)

    • [Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Yoweli.]

    • Yow. 2:28, 29​—Akhristu odzozedwa amagwira ntchito monga aneneri a Yehova (w02 8/1 15 ¶4-5; jd 167 ¶4)

    • Yow 2:30-32​—Okhawo amene amaitanira pa dzina la Yehova ndi amene adzapulumuke pa tsiku lake la chiweruzo (w07 10/1 13 ¶2)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yow. 2:12, 13​—Kodi mavesi amenewa akutiphunzitsa chiyani pa nkhani ya kulapa mochokera pansi pa mtima? (w07 10/1 13 ¶5)

    • Yow 3:14​—Kodi ‘chigwa choweruzira mlandu’ n’chiyani? (w07 10/1 13 ¶3)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yow. 2:28–3:8

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG., limene munagawira pa ulendo woyamba. Pomaliza mufotokozereni za vidiyo iliyonse ya pa jw.org.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 197 ¶3-5

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 91

  • Yehova Amatithandiza Kuti Tipirire Mayesero: (9 min.) Onetsani vidiyo yakuti Yehova Ndi Nsanja Yanga Yolimba. Kenako funsani omvetsera mafunso awa: Kodi banja la a Henschel linakumana ndi mayesero otani? Kodi kukhulupirika kwa makolo kumathandiza bwanji ana? Kodi Yehova angakulimbikitseni bwanji ngati mmene anachitira ndi M’bale Henschel?

  • Khalani Bwenzi la Yehova​—Dzina la Yehova: (6 min.) Onetsani vidiyo yakuti Khalani Bwenzi la Yehova​—Dzina la Yehova. Kenako pemphani ana amene munawasankhiratu kuti abwere kupulatifomu ndipo muwafunse mafunso otsatirawa: Kodi dzina la Yehova limatanthauza chiyani? Kodi Yehova analenga zinthu ziti? Kodi Yehova angakuthandize bwanji iweyo?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 9 ¶10-15, komanso tsamba 90, 93, 96-97

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 72 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena