Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 November tsamba 4
  • November 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • November 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 November tsamba 4

November 13-19

OBADIYA 1–YONA 4

  • Nyimbo Na. 42 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muziphunzirapo Kanthu pa Zimene Munalakwitsa”: (10 min.)

    • [Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Obadiya.]

    • [Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Yona.]

    • Yona 3:1-3​—Yona anaphunzirapo kanthu pa zimene analakwitsa (ia 114 ¶22-23)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Obad. 10​—Kodi mawu akuti Edomu ‘sadzakhalaponso mpaka kalekale’ anakwaniritsidwa bwanji? (w07 11/1 13 ¶5)

    • Obad. 12​—Kodi tikuphunzirapo chiyani pa zimene Mulungu ananena podzudzula Aedomu? (jd 112 ¶4-5)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yona 3:1-10

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) wp17.6 chikuto​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) wp17.6 chikuto​—Pitirizani kukambirana zokhudza magazini imene munamupatsa kale. Musonyezeni limodzi mwa mabuku amene timagwiritsa ntchito pophunzira Baibulo.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) ld 12-13​—Sankhani zithunzi zoti mukambirane.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 37

  • “Zimene Tikuphunzira Kuchokera m’Buku la Yona”: (15 min.) Yambani ndi kuonetsa vidiyo yakuti Kulambira kwa Pabanja: Yona Anaphunzirapo Kanthu pa Chifundo cha Yehova.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 10 ¶1-7 komanso tsamba 98 ndi 99

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 133 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena