Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 January tsamba 6
  • January 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • January 22-28
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 January tsamba 6

January 22-28

MATEYU 8-9

  • Nyimbo Na. 17 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yesu Ankakonda Anthu”: (10 min.)

    • Mat. 8:1-3​—Yesu anachitira chifundo munthu wodwala khate (“kumukhudza” ”Ndikufuna” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 8:3, nwtsty)

    • Mat. 9:9-13​—Yesu ankakonda anthu omwe ankanyozedwa ndi ena (“kudya patebulo” “okhometsa msonkho” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 9:10, nwtsty)

    • Mat. 9:35-38​—Kukonda anthu kunachititsa kuti Yesu azilalikira uthenga wabwino ngakhale atatopa ndiponso anapempha Mulungu kuti atumize antchito ambiri oti agwire ntchitoyi (“anawamvera chisoni” mfundo zimene ndikuphunzira pa Mat. 9:36, nwtsty)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mat. 8:8-10​—Kodi tingaphunzire chiyani pa zimene Yesu anakambirana ndi mkulu wa asilikali? (w02 8/15 13 ¶16)

    • Mat. 9:16, 17​—Kodi Yesu ankatanthauza chiyani pofotokoza mafanizo awiriwa? (jy 70 ¶6)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mat. 8:1-17

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene. Muitanireni ku misonkhano yathu.

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 3 min.) Sankhani lemba komanso buku limene mukufuna kugwiritsa ntchito.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 47 ¶18-19

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 145

  • ‘Mulungu Anamuika Kukhala Ambuye ndi Khristu’​—Mbali Yoyamba​—Mbali ina ya vidiyoyi: (15 min.) Nkhani yokambirana. Werengani Mateyu 9:18-25, kenako onerani mbali ya vidiyoyi. Mukamaliza kambiranani mafunso otsatirawa:

    • Kodi Yesu anasonyeza bwanji chifundo kwa Yairo komanso mzimayi wina yemwe ankadwala?

    • Kodi nkhaniyi yakuthandizani bwanji kukhulupirira maulosi a m’Baibulo onena zimene zidzachitike Ufumu wa Mulungu ukamadzalamulira?

    • Kodi tingatsanzire Yesu pa nkhani yokonda anthu m’njira zina ziti?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 13 ¶11-23

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 95 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena