Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsamba 5
  • May 21-27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 21-27
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 May tsamba 5

May 21-27

MALIKO 11-12

  • Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Anaponya Zochuluka Kuposa Onse”: (10 min.)

    • Maliko 12:41, 42​—Yesu anaona mkazi wamasiye akuponya makobidi awiri aang’ono moponyamo zopereka (“moponyamo zopereka” “timakobidi tiwiri tating’ono” mfundo zimene ndikuphunzira pa Maliko 12:41, 42, nwtsty)

    • Maliko 12:43​—Yesu anayamikira kwambiri zimene mayiyu anachita ndipo anafotokozera ophunzira ake (w97 10/15 16-17 ¶16-17)

    • Maliko 12:44​—Zimene mayiyu anapereka zinali zamtengo wapatali kwa Yehova (w97 10/15 17 ¶17; w87 12/1 30 ¶1; cl 185 ¶15)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Maliko 11:17​—N’chifukwa chiyani Yesu ananena kuti kachisi ndi “nyumba yopemphereramo mitundu yonse”? (“nyumba yopemphereramo mitundu yonse” mfundo zimene ndikuphunzira pa Maliko 11:17, nwtsty)

    • Maliko 11:27, 28​—Kodi “zinthu” zomwe anthu otsutsa Yesuwa ankanena ndi ziti? (jy 244 ¶7)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Maliko 12:13-27

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene. Sonyezani mmene mungayankhire pa nkhani inayake yomwe anthu a m’gawo lanu amatsutsa kawirikawiri.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene. Munthuyo wakufotokozerani kuti wachibale wake wamwalira posachedwapa.

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 118

  • Kukhulupirira Yehova Kumathandiza Kuti Zinthu Zitheke: (15 min.) Onerani vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 18 ¶9-20 komanso tsamba 199, 200-201

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 98 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena