Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsamba 2
  • July 2-8

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 2-8
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 July tsamba 2

July 2-8

Luka 6-7

  • Nyimbo Na. 109 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muzikhala Owolowa Manja”: (10 min.)

    • Luka 6:37​—Ngati tikufuna kuti anthu ena azitikhululukira, ifenso tizikhululuka (“Pitirizani kukhululukira anthu machimo awo ndipo machimo anunso adzakhululukidwa” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 6:37, nwtsty; w08 5/15 9-10 ¶13-14)

    • Luka 6:38​—Tizikhala ndi chizolowezi chogawira ena zinthu (“Khalani opatsa” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 6:38, nwtsty)

    • Luka 6:38​—Muyezo umene tikuyezera ena, iwonso adzatiyezera womwewo (“m’matumba anu” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 6:38, nwtsty)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Luka 6:12, 13​—Kodi Akhristu amene akufuna kupanga zosankha zikuluzikulu angatsanzire bwanji Yesu? (w07 8/1 6 ¶1)

    • Luka 7:35​—Kodi mawu a Yesu palembali angatithandize bwanji ngati ena akutinenera zoipa? (“zotsatira zake” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 7:35, nwtsty)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Luka 7:36-50

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha zimene tinganene.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bhs 198 ¶4-5

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 108

  • Muzitsanzira Yehova Pokhala Owolowa Manja: (15 min.) Onerani vidiyoyi. Kenako kambiranani mafunso otsatirawa:

    • Kodi Yehova ndi Yesu amasonyeza bwanji kuti ndi owolowa manja?

    • Kodi Yehova amatidalitsa bwanji tikakhala owolowa manja?

    • Kodi tingasonyeze bwanji kuti ndife owolowa manja pa nkhani yokhululukira ena?

    • Kodi tingasonyeze bwanji kuti ndife owolowa manja pa nkhani ya mmene timagwiritsira ntchito nthawi yathu?

    • Kodi tingasonyeze bwanji kuwolowa manja pa nkhani yoyamikira ena?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 21 ¶1-7 komanso tsamba 220-221

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 57 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena