Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 July tsamba 6
  • July 30–August 5

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 30–August 5
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 July tsamba 6

July 30–August 5

Luka 14-16

  • Nyimbo Na. 125 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Fanizo la Mwana Wolowerera”: (10 min.)

    • Luka 15:11-16​—Mwana wolowerera anawononga cholowa chake pochita makhalidwe oipa (“Munthu wina anali ndi ana aamuna awiri” “Wamng’ono” “anasakaza” “m’makhalidwe oipa” “kuti azikaweta nkhumba” “chakudya cha nkhumba” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 15:11-16, nwtsty)

    • Luka 15:17-24​—Iye anadzimvera chisoni ndipo bambo ake anamuchitira chifundo n’kumulandiranso (“ndachimwira inu” “aganyu” “anamupsompsona mwachikondi” “kutchedwa mwana wanu” “mkanjo . . . mphete . . . nsapato” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 15:17-24, nwtsty)

    • Luka 15:25-32​—Bambo anathandiza mwana wake wamkulu kuti ayambe kuona zinthu moyenera

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Luka 14:26​—Kodi mawu akuti ‘kudana’ pavesili akutanthauza chiyani? (“osadana” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 14:26, nwtsty)

    • Luka 16:10-13​—Kodi Yesu ankatanthauza chiyani pamene ananena za “chuma chosalungama”? (w17.07 8-9 ¶7-8)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Luka 14:1-14

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene. Kenako muitanireni kumisonkhano yathu.

  • Ulendo Wobwereza Wachitatu: (Osapitirira 3 min.) Sankhani lemba lililonse ndipo gawirani buku kapena kabuku kamene timagwiritsa ntchito pophunzira ndi anthu.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 32 ¶14-15

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 107

  • “Mwana Wolowerera”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Yambani ndi kuonera mbali ina ya vidiyo yakuti Mwana Wolowerera.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 22 ¶8-16

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 139 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena