Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 August tsamba 5
  • August 20-26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 20-26
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 August tsamba 5

August 20-26

Luka 21-22

  • Nyimbo Na. 27 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chipulumutso Chanu Chikuyandikira”: (10 min.)

    • Luka 21:25​—Pa chisautso chachikulu padzachitika zinthu zochititsa mantha (kr 226 ¶9)

    • Luka 21:26​—Adani a Yehova adzasowa chochita

    • Luka 21:27, 28​—Yesu akadzabwera adzapulumutsa anthu okhulupirika (w16.01 10-11 ¶17; w15 7/15 17 ¶13)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Luka 21:33​—Kodi mawu a Yesu palembali akutanthauza chiyani? (“Kumwamba ndi dziko lapansi zidzachoka” “mawu anga sadzachoka ayi” mfundo zimene ndikuphunzira pa Luka 21:33, nwtsty)

    • Luka 22:28-30​—Kodi ndi pangano liti limene Yesu anakhazikitsa ndipo anapangana ndi ndani, nanga lidzakwaniritsa chiyani? (w14 10/15 16-17 ¶15-16)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Luka 22:35-53

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene. Kenako sonyezani mmene mungayankhire pa nkhani inayake yomwe anthu a m’gawo lanu amatsutsa kawirikawiri.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha zimene tinganene. Kenako sonyezani zimene mungachite ngati mwininyumba ali wotanganidwa.

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 136

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 1

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 96 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena