Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 January tsamba 8
  • Yehova Anatithandiza Kulera Ana Athu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Anatithandiza Kulera Ana Athu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Makolo Ayenera Kuphunzitsa Ana Awo Kukonda Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Ukapanda Kudyerera Ubwana Wako
    Galamukani!—2003
  • Mungatani Kuti Aliyense Azisangalala M’banja Lanu?​—Mbali Yachiwiri
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Makolo, Muzithandiza Ana Anu Kuti Azikonda Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 January tsamba 8
A Abilio ndi a Ulla Amorim

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Yehova Anatithandiza Kulera Ana Athu

Kodi makolo angaphunzire chiyani kuchokera kwa Atate wathu Yehova, zomwe zingawathandize kuti alere bwino ana awo? Onerani vidiyo yakuti Yehova Anatithandiza Kulera Ana Athu, yonena za banja la a Abilio ndi a Ulla Amorim ndipo kenako yankhani mafunso otsatirawa:

A Abilio ndi a Ulla Amorim pa tsiku la ukwati wawo, ali ndi ana awo, mwana wawo wamwamuna ndi mkazi wake ali mu utumiki
  • Kodi kuganizira mmene makolo awo anawalerera kunathandiza bwanji a Abilio ndi a Ulla kuti alere bwino ana awo?

  • Kodi ana awo amakumbukira zinthu zosangalatsa ziti zimene zinkachitika ali aang’ono?

  • Kodi a Abilio ndi a Ulla anagwiritsa ntchito bwanji mfundo za pa Deuteronomo 6:6, 7?

  • N’chifukwa chiyani iwo sankangouza ana awo malamulo oti azitsatira?

  • Kodi anathandiza bwanji ana awo kuti paokha akonze tsogolo lawo?

  • Ndi zinthu ziti zimene anadzimana chifukwa cholimbikitsa ana awo kuchita utumiki wa nthawi zonse? (bt 178 ¶19)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena