Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 4
  • July 15-21

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 15-21
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 4

July 15-21

2 ATESALONIKA 1-3

  • Nyimbo Na. 67 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Wosamvera Malamulo Adzaonekera”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la 2 Atesalonika.]

    • 2 Ates. 2:6-8​—‘Wosamvera malamulo,’ yemwe ankasocheretsa anthu, anali woti adzaonekera (it-1 972-973)

    • 2 Ates. 2:9-12​—Anthu omwe asocheretsedwa ndi ‘wosamvera malamulo’ adzaweruzidwa (it-2 245 ¶7)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • 2 Ates. 1:7, 8​—Kodi Baibulo limatanthauza chiyani likamanena kuti Yesu ndi angelo ake adzaonekera “m’moto walawilawi”? (it-1 834 ¶5)

    • 2 Ates. 2:2​—Kodi m’vesili, Paulo ankatanthauza chiyani ponena kuti “mawu ouziridwa”? (it-1 1206 ¶4)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) 2 Ates. 1:1-12 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 6)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba, kenako musonyezeni buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa. (th phunziro 12)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 61

  • Kodi Utumiki Wanu Mumangouchita Mwamwambo Chabe?: (15 min.) Onerani vidiyo yakuti, Muziikirapo Mtima pa Utumiki Wanu.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 43 ndime 8-18

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 64 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena