Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 January tsamba 5
  • “Anachitadi Momwemo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Anachitadi Momwemo”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • “Nowa Anayenda ndi Mulungu Woona”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • “Anayenda Ndi Mulungu Woona”
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • Chikhulupiriro cha Nowa Chimatsutsa Dziko Lapansi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Anapulumutsidwa “Pamodzi ndi Anthu Ena 7”
    Nsanja ya Olonda—2013
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 January tsamba 5
Nowa ndi mwana wake akumanga chingalawa, mwanayo wakwera pamakwerero a katawala ndipo akupaka phula chingalawacho.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 6-8

“Anachitadi Momwemo”

6:9, 13-16, 22

Taganizirani ntchito imene Nowa ndi banja lake anali nayo kuti amange chingalawa popanda zipangizo komanso njira zamakono zomangira.

  • Chingalawacho chinali chachikulu kwambiri. Chinali cha mamita 133 m’litali, mamita 22 m’lifupi komanso mamita 13 kupita m’mwamba

  • Ankafunika kugwetsa mitengo, kuidula, kenako n’kuipititsa kumene ankagwirira ntchito

  • Ankafunika kupaka phula mkati komanso kunja kwa chingalawacho

  • Ankafunikanso kusunga chakudya cha chaka chathunthu cha iyeyo ndi banja lake komanso zinyama

  • Ntchitoyi iyenera kuti inatenga zaka 40 kapena 50 kuti ithe

Kodi nkhaniyi ingatithandize bwanji ngati timaona kuti n’zovuta kuchita zimene Yehova amatiuza?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena