Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 6
  • Yosefe Anasonyeza Kudziletsa Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yosefe Anasonyeza Kudziletsa Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • “Kodi Ine Ndatenga Malo a Mulungu?”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Ankasamalira Banja Lake Komanso Anakhalabe Wokhulupirika
    Tsanzirani Chikhulupiriro Chawo
  • ‘Ndingachitirenji Choipa Chachikulu N’kuchimwira Mulungu?’
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Ankateteza ndi Kusamalira Banja Lake Komanso Anakhalabe Wokhulupirika
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 6
Yosefe akulira ndipo azichimwene ake ali kumbuyo kwake.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 42-43

Yosefe Anasonyeza Kudziletsa Kwambiri

42:5-7, 14-17, 21, 22

Kodi mukuganiza kuti Yosefe anamva bwanji atakumana ndi azichimwene ake mosayembekezereka? Iye akanatha kudzidziwikitsa kwa azichimwene akewo nthawi yomweyo kenako n’kuwakumbatira, kapena akanatha kuwabwezera zachipongwe zomwe anamuchitira. Koma sanachite zinthu mopupuluma. Ndiye kodi inuyo mungatani ngati anthu a m’banja lanu kapena anthu ena atakuchitirani zinthu zopanda chilungamo? Chitsanzo cha Yosefe chikutiphunzitsa kufunika kokhala odziletsa komanso kuchita zinthu modekha m’malo motsatira mtima wathu wonyenga n’kumachita zinthu mopupuluma.

Kodi mungatsanzire bwanji Yosefe pa mavuto amene mumakumana nawo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena