Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsamba 3
  • July 13-19

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 13-19
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 July tsamba 3

July 13-19

EKISODO 8-9

  • Nyimbo Na. 12 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Farao Yemwe Anali Wonyada Anathandiza Kukwaniritsa Cholinga cha Mulungu Mosadziwa”: (10 min.)

    • Eks 8:15​—Farao anaumitsa mtima wake ndipo sanamvere Mose ndi Aroni (it-2 1040-1041)

    • Eks 8:18, 19​—Farao anaumitsabe mtima wake ngakhale kuti ochita zamatsenga ake anavomereza kuti sangathe kuchita zimene Yehova anachita

    • Eks 9:15-17​—Mwa kulola Farao kukhalabe ndi moyo, Yehova anachititsa kuti dzina lake lilemekezedwe (it-2 1181 ¶3-5)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 8:21​—Kodi tizilombo totchulidwa palembali tinali toopsa bwanji? (it-1 878)

    • Eks 8:25-27​—N’chifukwa chiyani Mose ananena kuti nsembe za Aisiraeli zikanakhala “chonyansa cha Aiguputo”? (w04 3/15 25 ¶9)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 8:1-19 (th phunziro 12)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi, ndipo kenako funsani mafunso otsatirawa: Kodi wofalitsayu anatani mwininyumba atasonyeza kuti sakufuna kukambirana naye? Kodi wofalitsayu akanatani kuti agawire buku kapena kabuku kopezeka pa Zinthu Zophunzitsira?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 6)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 3)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako m’patseni buku kapena kabuku kamene timagwiritsa ntchito pophunzira ndi anthu. (th phunziro 12)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 74

  • “Muzidzichepetsa​—Muzipewa Kudzitama”: (7 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Khalani Bwenzi la Yehova​—Uzidzichepetsa. Kenako itanani ana omwe munawasankhiratu kuti abwere kutsogolo ndipo muwafunse mafunso okhudza vidiyoyi.

  • “Muzidzichepetsa Ena Akamakuyamikirani”: (8 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muzikhala Okhulupirika Ngati Mmene Yesu Analili​—Pamene Anthu Ena Akukuyamikirani.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 91

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 151 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena