Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 September tsamba 2
  • September 7-13

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 7-13
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 September tsamba 2

SEPTEMBER 7-13

EKISODO 23-24

  • Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Musamatsatire Khamu la Anthu”: (10 min.)

    • Eks 23:1​—Musamafalitse nkhani zabodza zimene mwamva (w18.08 4 ¶7-8)

    • Eks 23:2​—Musamatengeke ndi anthu kuti muchite zoipa (it-1 11 ¶3)

    • Eks 23:3​—Musamakondere (it-1 343 ¶5)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 23:9​—Kodi Yehova anawauza chiyani Aisiraeli pofuna kuwathandiza kuti azisonyeza chifundo? (w16.10 9 ¶4)

    • Eks 23:20, 21​—Kodi pali umboni wotani wosonyeza kuti mngelo wotchulidwa mulembali ndi Mikayeli? (it-2 393)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 23:1-19 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Mwininyumba atayankha molakwika, kodi wofalitsa ananena zotani kuti apitirize kukambirana naye? Kodi wofalitsayu akananenanso zotani kuti agawire Nsanja ya Olonda yogawira Na. 3 2020?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musonyezeni ndi kukambirana naye mfundo za m’vidiyo yakuti N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? (koma musaonetse vidiyoyi). (th phunziro 1)

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w16.05 30-31​—Mutu: Kodi Mkhristu Angadziwe Bwanji Ngati N’zoyenera Kupereka Ndalama kwa Ogwira Ntchito M’boma? (th phunziro 14)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 124

  • “Musamafalitse Nkhani Zabodza”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yamakatuni yakuti Kodi Ndingatani Kuti Ndithetse Miseche?

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (Osapitirira 30 min.) jy mutu 99

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 85 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena