Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 September tsamba 14
  • October 25-31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 25-31
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 September tsamba 14

October 25-31

YOSWA 15-17

  • Nyimbo Na. 146 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Muziteteza Cholowa Chanu Chomwe Ndi Chamtengo Wapatali”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yos 17:15, 18​—Kodi tikudziwa bwanji kuti ku Isiraeli kunali mitengo yambiri? (w15 7/15 32)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yos 15:1-12 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 19)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni chimodzi mwa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 4)

  • Phunziro la Baibulo: (5 min.) lffi phunziro 01 mfundo 6 komanso Zimene Ena Amanena (th phunziro 9)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 139

  • “Muzilalikira Uthenga Wabwino Wakuti Dziko Labwino Layandikira”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya nyimbo yakuti Dziko Latsopano Lomwe Likubwera.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lvs mutu 6 ndime 20-23, mfundo za m’Baibulo tsa. 86-88

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 94 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena