Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsamba 9
  • October 3-9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 3-9
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 September tsamba 9

October 3-9

1 MAFUMU 17-18

  • Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Mukayikakayika Mpaka Liti?”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • 1Mf 18:1​—N’chifukwa chiyani Yesu ananena kuti chilala cha m’nthawi ya Eliya chinatenga “zaka zitatu ndi miyezi 6”? (Lu 4:25; w08 4/1 19, bokosi)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) 1Mf 18:36-46 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo ya Ulendo Woyamba: Baibulo​—2Ti 3:16, 17. Muziimitsa vidiyoyi nthawi iliyonse imene pali chizindikiro chosonyeza kuti muime n’kufunsa omvera mafunso omwe ali muvidiyoyi.

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Gwiritsani ntchito nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 12)

  • Nkhani: (5 min.) w14 2/15 14-15​—Mutu: Kodi Tingaphunzire Chiyani pa Chikhulupiriro cha Mkazi Wamasiye? (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 111

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 21

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 83 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena