Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 September tsamba 15
  • Kufikira Pamene Adzakhalenso Ndi Moyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kufikira Pamene Adzakhalenso Ndi Moyo
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Mungachite Mukaferedwa
    Nkhani Zina
  • Chiphunzitso cha Kuuka kwa Akufa Chimakukhudzani
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Kodi Yesu Atafa Anakulungidwa mu Nsalu ya Maliro Yomwe Inasungidwa ku Turin?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Kodi Chiyembekezo cha Kuuka kwa Akufa Mumachiona Motani?
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 September tsamba 15
Mayi wakumbatira mwana wake amene waukitsidwa m’Paradaiso.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kufikira Pamene Adzakhalenso Ndi Moyo

Munthu amene timam’konda akamwalira timatonthozedwa tikaganizira kuti adzaukitsidwa. Ngakhale zili choncho, uchimo komanso imfa zili ngati chophimba chimene chimatiphimba tonsefe ndipo chimatisowetsa mtendere. (Yes 25:7, 8) N’chifukwa chake “chilengedwe chonse chikubuula limodzi ndi kumva zowawa.” (Aro 8:22) Kodi tingatani kuti tipirire imfa ya okondedwa athu kufikira pamene adzakhalenso ndi moyo? M’Mawu a Mulungu muli mfundo zimene zingatithandize.

ONERANI VIDIYO YAKUTI ZIMENE MUNGACHITE MUKAFEREDWA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Danielle komanso Masahiro ndi Yoshimi anakumana ndi mavuto otani?

  • Kodi mfundo 5 zotchulidwa mu vidiyoyi zinawathandiza bwanji?

  • Kodi ndi ndani amene amatitonthoza?​—2Ak 1:3, 4

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena