Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 July tsamba 6-7
  • July 21-27

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 21-27
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 July tsamba 6-7

JULY 21-27

MIYAMBO 23

Nyimbo Na. 97 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Mfundo Zothandiza pa Nkhani ya Mowa

(10 min.)

Ngati mwasankha kuti muzimwa mowa, musamamwe wambiri (Miy 23:20, 21; w04 12/1 19 ¶5-6)

Muzikumbukira kuipa koledzera (Miy 23:29, 30, 33-35; it-1 656)

Musamapusitsike ndi maganizo akuti mowa si woipa (Miy 23:31, 32)

Mlongo wakhala pampando ndipo akuyang’ana botolo la mowa.

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 23:21—Kodi pali kusiyana kotani pakati pa kususuka ndi kunenepa? (w04 11/1 31 ¶2)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 23:1-24 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(2 min.) KULALIKIRA M’MALO OPEZEKA ANTHU AMBIRI. (lmd phunziro 3 mfundo 5)

5. Ulendo Wobwereza

(5 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. M’pempheni kuti mumuonetse mmene phunziro la Baibulo limachitikira. (lmd phunziro 9 mfundo 5)

6. Kuphunzitsa Anthu

(5 min.) Limbikitsani wophunzira wanu amene akulimbana ndi chizolowezi chimene Baibulo limaletsa. (lmd phunziro 12 mfundo 4)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 35

7. Kodi Padzakhale Mowa Kapena Ayi?

(8 min.) Nkhani yokambirana.

Kodi anthu amene akukonza zochitika zinazake, mwachitsanzo phwando la ukwati, akuyenera kukonza zoti padzakhale mowa? Chimenechi ndi chosankha cha aliyense payekha. Koma munthu asanasankhe zoyenera kuchita pa nkhani imeneyi, akuyenera kuganizira mofatsa mfundo zingapo za m’Baibulo komanso zinthu zina.

Anthu amene ali pachibwenzi akukambirana ngati pa ukwati wawo padzakhale mowa. Patebulo pali Baibulo komanso tabuleti yomwe pakuoneka mabotolo a mowa.

Onerani VIDIYO yakuti Kodi Padzakhale Mowa Kapena Ayi? Kenako funsani mafunso awa:

  • Kodi mfundo za m’Baibulo zotsatirazi zingathandize bwanji anthu amene akukonza phwando kuganizira ngati pakuyenera kukakhala mowa kapena ayi?

    • Yoh 2:9—Yesu anasandutsa madzi kukhala vinyo pa phwando la ukwati.

    • 1Ak 6:10—‘Zidakwa sizidzalowa mu Ufumu wa Mulungu.’

    • 1Ak 10:31, 32—“Kaya mukudya kapena kumwa . . . , muzichita zinthu zonse kuti zibweretse ulemerero kwa Mulungu. Muzipewa kukhumudwitsa.”

  • Kodi ndi zinthu zina ziti zimene mukuyenera kuziganizira?

  • Kuti tizisankha zinthu mwanzeru, n’chifukwa chiyani timafunika kugwiritsa ntchito “luso la kuganiza” n’cholinga choti tikwanitse kusankha mfundo za m’Baibulo zimene tingagwiritse ntchito?—Aro 12:1; Mla 7:16-18

8. Zofunika Pampingo

(7 min.)

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) lfb mutu 2, mawu ofotokoza chigawo 2 komanso mutu 3

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 40 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena