Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w20 August tsamba 1-32
  • Nsanja ya Olonda Yophunzira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Nsanja ya Olonda Yophunzira
  • Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2020
w20 August tsamba 1-32
The Watchtower Study Edition, August 2020.

Nsanja ya Olonda Yophunzira

AUGUST 2020

NKHANI ZOPHUNZIRA: SEPTEMBER 28–NOVEMBER 1, 2020

© 2020 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

Magaziniyi sitigulitsa. Timaipereka ngati njira imodzi yophunzitsira anthu Baibulo padziko lonse ndipo ndalama zoyendetsera ntchitoyi ndi zimene anthu amapereka mwa kufuna kwawo. Ngati mukufuna kupereka pitani pa donate.jw.org.

Malemba onse m’magaziniyi akuchokera mu Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika lolembedwa m’Chichewa chamakono, kupatulapo ngati tasonyeza Baibulo lina.

CHITHUNZI CHAPACHIKUTO:

Yesu ali kumwamba, kumbuyo kwake kuli olamulira anzake omwe akuyang’ana angelo ambirimbiri. Angelo ena akupita padziko lapansi kuti akagwire ntchito imene apatsidwa. Yehova amapereka zochita kwa onse amene akusonyezedwa pachithunzichi (Onani nkhani yophunzira 32, ndime 5)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena