Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g91 11/8 tsamba 14
  • Kodi Nchifukwa Ninji “Kunyengererako”?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Nchifukwa Ninji “Kunyengererako”?
  • Galamukani!—1991
  • Nkhani Yofanana
  • Tetezani Maganizo Anu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kupotoza Nkhani
    Galamukani!—2000
  • Nkhani Zokopa Zingaphetse Anthu
    Galamukani!—2000
  • Musanyengedwe ndi Nkhani Zokopa!
    Galamukani!—2000
Onani Zambiri
Galamukani!—1991
g91 11/8 tsamba 14

Kodi Nchifukwa Ninji “Kunyengererako”?

Mu 1622, Pope Gregory XV anakhazikitsa mpingo, kapena komiti, ya makadinala 13, atsogoleri apamwamba achipembedzo 2 ndi mlembi kukayang’anira amishonale a Tchalitchi cha Roma Katolika. Iye anautcha kukhala Congregatio de Propaganda Fide—Mpingo Wofalitsa Chikhulupiriro—kapena mwachidule Propaganda (Kunyengerera). M’kupita kwanthaŵi liwu limeneli linafikira kutanthauza kuyesayesa kulikonse kwa kufalitsa malingaliro kapena zikhulupiriro kuchitira kutembenuza anthu.

Tsopano, liwulo “kunyengerera” kaŵirikaŵiri limagwirizanitsidwa ndi kuipitsa zenizeni, kusonkhezera monyenga malingaliro a anthu, mwachitsanzo monga m’nthaŵi za nkhondo. Koma olamulira ena amalingalira kuti kutsatsa malonda kwabwino kwambiri kungafotokozedwe bwino lomwe kukhala kunyengerera, makamaka ngati kukuphatikizapo kupseterera. The World Book Encyclopedia likuthirira ndemanga kuti: Aphunzitsi m’zitaganya zademokrase amaphunzitsa anthu mmene angalingalilire, koma onyengerera amaŵauza zoti alingalire.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena