Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 1/06 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2006
  • Nkhani Yofanana
  • Michael Agricola “Anasintha Zinthu Kwambiri”
    Galamukani!—2006
  • N’chifukwa Chiyani Ndimadzivulaza?
    Galamukani!—2006
  • Kodi Ndingatani Kuti Ndisiye Kudzivulaza?
    Galamukani!—2006
  • Kuchokera kwa Owerenga
    Galamukani!—2006
Onani Zambiri
Galamukani!—2006
g 1/06 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2006

Kodi M’tsogolo Muli Zotani?

Kodi munayamba mwaganizirapo kuti dzikoli lidzakhala lotani zaka 10, 20, kapena kuposerapo m’tsogolomu? Baibulo limapereka zifukwa zogwira mtima zotithandiza kukhulupirira kuti m’tsogolomu tidzasangalala kwambiri kuposa kale lonse.

3 Kwa Owerenga

5 Kodi Tili ndi Tsogolo Labwino?

6 Kodi Dzikoli Likulowera Kuti?

13 Nkhungu Imathandiza Komanso Imawononga

16 Basi Adutsa!

18 Zimene Baibulo Limanena

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kudalira Baibulo Kuti Lizititsogolera?

20 Zochitika Padzikoli

21 Michael Agricola “Anasintha Zinthu Kwambiri”

24 Maselo Ofiira a M’magazi Ndi Odabwitsa Kwambiri

30 Kuchokera kwa Owerenga

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Mwana Akamwalira

N’chifukwa Chiyani Ndimadzivulaza? 10

Werengani za anthu amene akuvutika chifukwa chodzivulaza, chizolowezi chomwe chimatchedwanso kudzicheka, ndipo werenganinso zifukwa zimene amachitira zimenezi.

Chikhulupiriro Chandithandiza Kupirira Matenda Oopsa 25

Werengani nkhani ya mnyamata wina amene wakhala moyo wosangalala ndiponso waphindu, ngakhale kuti ali ndi matenda amene anam’pheratu ziwalo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena