Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 1/07 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2007
  • Nkhani Yofanana
  • Aliyense Akufuna Moyo Wathanzi!
    Galamukani!—2007
  • Matenda Onse Adzatha!
    Galamukani!—2007
  • Malo a Zachilengedwe a Belize Barrier Reef—Chuma Chadziko Lonse
    Galamukani!—2007
  • Nowa Akhoma Chingalawa
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Galamukani!—2007
g 1/07 tsamba 1-2

Zamkatimu

January 2007

Matenda Onse Adzatha!

Sayansi yapititsa patsogolo kwambiri ntchito zachipatala ndiponso zolimbana ndi matenda. Komabe, anthu akupitiriza kuvutika ndi matenda. Kodi idzafika nthawi imene matenda onse adzathe?

3 Aliyense Akufuna Moyo Wathanzi!

4 Kodi Sayansi Idzathetsa Matenda Onse?

10 Matenda Onse Adzatha!

12 Mfumu Imene Inafunafuna Nzeru

15 Zochitika Padzikoli

16 Taonani Bwenzi la Alimi—Chikumbu

18 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Chikhristu Chalephera Kusintha Zinthu?

23 Malo a Zachilengedwe a Belize Barrier Reef—Chuma Chadziko Lonse

31 Kodi Mungayankhe Bwanji?

32 Kutonthoza Amene Akulira

Chingalawa cha Nowa Chinapangidwa Mwaluso 20

Katswiri wolemba mapulani a kapangidwe ka sitima zapamadzi watulukira kuti chingalawa cha Nowa chinapangidwa mogwirizana kwambiri ndi mapulani amakono a kapangidwe ka sitima.

Kodi Ndingayambe Chibwenzi Nditafika Msinkhu Wotani? 27

Kodi ndinu wokonzeka kuyamba chibwenzi? Taonani mfundo zitatu zimene zingakuthandizeni kuyankha funso limeneli.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena